Oweruza 7:14 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo mnzace anayankha nati, Ici si cina konse koma lupanga la Gideoni mwana wa Yoasi, munthu wa Israyeli; Mulungu wapereka Midyani ndi a m'misasa onse m'dzanja lace.

Oweruza 7

Oweruza 7:7-15