Oweruza 15:14 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pamene anafika ku Leki Afilisti anapfuula pokomana naye; koma mzimu wa Yehova unamgwera kolimba, ndi zingwe zokhala pa manja ace zinanga bwazi lopserera ndi moto, ndi zomangira zace zinanyotsoka pa manja ace.

Oweruza 15

Oweruza 15:13-18