Oweruza 13:20 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pakuti kunali, pakukwera lawi la mota pa guwa la nsembe kumwamba, mthenga wa Yehova anakwera m'lawi la pa guwalo; ndi Manowa ndi mkazi wace ali cipenyere; nagwa iwowa nkhope zao pansi.

Oweruza 13

Oweruza 13:11-23