Oweruza 11:8 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo akuru a Gileadi ananena ndi Yefita, Cifukwa cace cakuti takubwerera tsopano ndico kuti umuke nafe ndi kucita nkhondo ndi ana a Amoni, nudzakhala mkuru wathu wa pa onse okhala m'Gileadi.

Oweruza 11

Oweruza 11:7-14