Oweruza 11:37 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo anati kwa atate wace, Andicitire ici, andileke miyezi iwiri, kuti ndicoke ndi kutsikira kumapiri, ndi kulirira unamwali wanga, ine ndi anzanga.

Oweruza 11

Oweruza 11:28-40