Oweruza 11:21 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Yehova Mulungu wa Israyeli anapereka Sihoni ndi anthu ace onse m'dzanja la Israyeli, ndipo anawakantha, ndi Israyeli analandira colowa cace, dziko lonse la Aamori, nzika za m'dziko lija.

Oweruza 11

Oweruza 11:18-22