Oweruza 11:2 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo mkazi wa Gileadi anambalira ana amuna; koma atakula ana amuna a mkaziyo anampitikitsa Yefita, nanena naye, Sudzalandira colowa m'nyumba ya atate wako; pakuti ndiwe mwana wa mkazi wina.

Oweruza 11

Oweruza 11:1-10