Nyimbo 7:12 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Tilawire kunka ku minda yamipesa;Tiyang'ane ngati mpesa waphuka, kunje ndi kuonetsa zipatso,Makangaza ndi kutuwa maluwa ace;Pompo ndidzakupatsa cikondi canga,

Nyimbo 7

Nyimbo 7:3-13