Nyimbo 6:12-13 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

12. Ndisanazindikire, moyo wanga unandiimikaPakati pa magareta a anthu anga aufulu.

13. Anati, Bwera, bwera, Msulamiwe;Bwera, bwera, tiyang'ane pa iwe.Muyang'aniranji pa Msulami,Ngati pa masewero akuguba?

Nyimbo 6