Nyimbo 5:15-16 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

15. Miyendo yace ikunga zoimiritsa za mwala wonyezimira,Zogwirika m'kamwa mwa golidi:Maonekedwe ace akunga Lebano, okometsetsa ngati mikungudza.

16. M'kamwa mwace muli mokoma: inde, ndiye wokondweretsa ndithu.Ameneyu ndi wokondedwa wanga, ameneyu ndi bwenzi langa,Ana akazi inu a ku Yerusalemu.

Nyimbo 5