Nyimbo 4:11 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

M'milomo yako, mkwatibwi, mukukha uci,Uci ndi mkaka ziri pansi pa lilime lako;Kununkhira kwa zobvala zako ndi kunga kununkhira kwa Lebano,

Nyimbo 4

Nyimbo 4:9-14