Nyimbo 1:6 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Musayang'ane pa ine, pakuti ndada,Pakuti dzuwa landidetsa.Ana amuna a amai anandikwiyira,Anandisungitsa minda yamipesa;Koma munda wanga wanga wamipesa sindinausunga.

Nyimbo 1

Nyimbo 1:1-11