Numeri 8:17 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pakuti a oyamba kubadwa onse mwa ana a Israyeli ndi anga, mwa anthu ndi zoweta; tsiku lija ndinakantha oyamba kubadwa onse m'dziko la Aigupto, ndinadzipatulira iwo akhale anga.

Numeri 8

Numeri 8:15-18