Numeri 20:27-29 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

27. Pamenepo Mose anacita monga adamuuza; ndipo anakwera m'phiri la Hori pamaso pa khamu lonse.

28. Ndipo Mose anabvula Aroni zobvala zace, nabveka Eleazara mwana wace; ndipo Aroni anafa pomwepo pamwamba pa phiri, Pamenepo Mose ndi Eleazara anatsika m'phirimo.

29. Pamene khamu lonse linaona kuti Aroni adamwalira, anamlira Aroni masiku makumi atatu, ndiyo mbumba yonse ya Israyeli.

Numeri 20