Numeri 2:3 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo iwo akumanga mahema ao ku m'mawa koturuka dzuwa ndiwo a mbendera ya cigono ca Yuda, monga mwa makamu ao; ndipo kalonga wa ana a Yuda ndiye Nahesoni mwana wa Aminadabu.

Numeri 2

Numeri 2:1-6