41. Koma m'mawa mwace khamu lonse la ana a Israyeli anadandaula pa Mose ndi Aroni, nati, Mwapha anthu a Yehova, inu.
42. Ndipo kunali, posonkhanidwa khamulo kutsutsana nao Mose ndi Aroni, kuti anaceukira cihema cokomanako; taonani, mtambo unaciphimba, ndi ulemerero wa Yehova unaoneka.
43. Ndipo Mose ndi Aroni anadza kukhomo kwa cihema cokomanako.
44. Ndipo Yehova ananena ndi Mose, nati,