Nehemiya 12:15-23 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

15. wa Harimu, Adina; wa Merayoti, Helikai;

16. wa Ido, Zekariya; wa Ginetoni, Mesulamu;

17. wa Abiya, Zikiri; wa Minyamini, wa Moadiya, Pilitai;

18. wa Biliga, Samura; wa Semaya, Yehonatani;

19. ndi wa Yoyaribi, Matani; wa Yedaya, Uzi;

20. wa Salai, Kalai; wa Amoki, Eberi;

21. wa Hilikiya, Hasabiya; wa Yedaya, Netaneli.

22. M'masiku a Ehasibi, Yoyada, Yohanana, ndi Yoduwa, Alevi analembedwa akuru a nyumba za makolo; ansembe omwe, mpaka ufumu wa Dariyo wa ku Perisiya.

23. Ana a Levi, akuru a nyumba za makolo, analembedwa m'buku la macitidwe, mpaka masiku a Yohanana mwana wa Eliasibu.

Nehemiya 12