Nehemiya 11:4 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo m'Yerusalemu munakhala ena a ana a Yuda ndi a ana a Benjamini. Mwa ana a Yuda: Ataya mwana wa Uziya, mwana wa Zekariya, mwana wa Amariya, mwana wa Sefatiya, mwana wa Mahalaleli, wa ana a Perezi;

Nehemiya 11

Nehemiya 11:1-7