Nehemiya 11:3 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Awa tsono ndi akulu a dziko okhala m'Yerusalemu; koma m'midzi ya Yuda yense anakhala pa colowa cace m'midzi mwao, ndiwo Israyeli, ansembe, ndi Alevi, ndi Anetini, ndi ana a akapolo a Solomo.

Nehemiya 11

Nehemiya 11:1-4