Mlaliki 5:1-3 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

1. Samalira phazi lako popita ku nyumba ya Mulungu; pakuti kuyandikira kumvera kupambana kupereka nsembe za zitsiru; pakuti sizizindikira kuti zirikucimwa.

2. Usalankhule mwanthuku mtima wako, usafulumire kunena kanthu pamaso pa Mulungu; pakuti Mulungu ali kumwamba, iwe uli pansi; cifukwa cace mau ako akhale owerengeka.

3. Pakuti loto lafika mwakucuruka nchito; ndipo mau a citsiru mwakucuruka maneno.

Mlaliki 5