Mlaliki 5:1 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Samalira phazi lako popita ku nyumba ya Mulungu; pakuti kuyandikira kumvera kupambana kupereka nsembe za zitsiru; pakuti sizizindikira kuti zirikucimwa.

Mlaliki 5

Mlaliki 5:1-3