13. Gwira mwambo, osauleka;Uusunge; pakuti ndiwo moyo wako.
14. Usalowe m'mayendedwe ocimwa,Usayende m'njira ya oipa.
15. Pewapo, osapitamo;Patukapo, nupitirire.
16. Pakuti akapanda kucita zoipa, samagona;Ndipo akapanda kukhumudwitsa wina, tulo tao tiwacokera.