Miyambi 30:14 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pali mbadwo mano ao akunga malupanga, zibwano zao zikunga mipeni;Kuti adye osauka kuwacotsa kudziko, ndi aumphawi kuwacotsa mwa anthu.

Miyambi 30

Miyambi 30:5-23