32. Pakuti wamphulupulu anyansa Yehova;Koma cinsinsi cace ciri ndi oongoka.
33. Mulungu atemberera za m'nyumba ya woipa;Koma adalitsa mokhalamo olungama.
34. Anyozadi akunyoza,Koma apatsa akufatsa cisomo.
35. Anzeru adzalandira ulemu colowa cao;Koma opusa adzakweza manyazi.