Miyambi 10:27-30 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

27. Kuopa Yehova kutanimphitsa masiku;Koma zaka za oipa zidzafinimpha,

28. Ciyembekezo ca olungama ndico cimwemwe;Koma cidikiro ca oipa cidzaonongeka.

29. Njira ya Yehova ndi linga kwa woongoka mtima;Koma akucita zoipa adzaonongeka.

30. Wolungama sadzacotsedwa konse:Koma oipa sadzakhalabe m'dziko.

Miyambi 10