Mika 3:6 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

cifukwa cace kudzakhala ngati usiku kwa inu, wopanda masomphenya; ndipo kudzadera inu, wopanda kulosa; ndi dzuwa lidzalowera aneneri, ndi usana udzawadera bii.

Mika 3

Mika 3:1-12