Mateyu 9:27 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo popita Yesu kucokera kumeneko, anamtsata Iye anthu awiri akhungu, opfuula ndi kuti, Muticitire ife cifundo, mwana wa Davide.

Mateyu 9

Mateyu 9:25-30