Mateyu 5:32 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

koma Ine ndinena kwa inu, kuti 4 yense wakucotsa mkazi wace, kosati cifukwa ca cigololo, amcititsa cigololo: ndipo amene adzakwata wocotsedwayo acita cigololo.

Mateyu 5

Mateyu 5:31-36