Mateyu 26:63 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Koma 4 Yesu anangokhala cete. Ndipo mkuru wa ansembe ananena kwa Iye, Ndikulumbiritsa Iwe pa Mulungu wamoyo, kuti utiuze ife ngati Iwe ndiwe Kristu, Mwana wa Mulungu.

Mateyu 26

Mateyu 26:62-72