Mateyu 23:30-33 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

30. ndi kuti, Ife tikadakhala m'masiku a makolo anthu, sitikadakhala oyanjana nao pa mwazi wa aneneri.

31. Pomwepo mutsimikiza nokha, kuti muli ana a iwo amene anapha aneneri.

32. Dzazani inu muyeso wa makolo anu.

33. Njoka inu, obadwa inu a mamba, mudzatha bwanji kuthawa kulanga kwace kwa gehena?

Mateyu 23