Mateyu 22:4-6 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

4. Pomwepo anatumizanso akapolo ena, nanena, Uzani oitanidwawo, Onani, ndakonza phwando langa; ng'ombe zanga, ndi zonona ndinazipha, ndi zinthu zonse zapsya: idzani kuukwati.

5. Koma iwo ananyalanyaza, nacoka, wina ku munda wace, wina ku malonda ace:

6. ndipo otsala anagwira akapolo ace, nawacitira cipongwe, nawapha.

Mateyu 22