Mateyu 20:11-13 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

11. Koma m'mene iwo analilandira, anaderera kwa mwini banja,

12. nati, Omarizira awa anagwira nchito mphindi yaing'ono, ndipo munawalinganiza ndi ife amene tinapirira kuwawa kwa dzuwa ndi: kutentha kwace.

13. Koma iye anayankha, nati kwa mmodzi wa iwo, Mnzanga, sindikunyenga iwe; kodi iwe sunapangana ndi ine pa rupiya latheka limodzi?

Mateyu 20