Mateyu 2:9 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo iwo, m'mene anamva mfumu, anamuka; ndipo onani, nyenyezi ija anaiona kum'mawa, inawatsogolera iwo, kufikira inadza niima pamwamba pomwe panali kamwanako.

Mateyu 2

Mateyu 2:5-18