Mateyu 12:49-50 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

49. Ndipo anatambalitsa dzanja lace pa ophunzira ace, nati, Penyani amai wanga ndi abale anga!

50. Pakuti 6 ali yense amene adzacita cifuniro ca Atate wanga wa Kumwamba, yemweyo ndiye mbale wanga, ndi mlongo wanga, ndi amai wanga.

Mateyu 12