Masalmo 99:6-9 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

6. Mwa ansembe ace muli Mose ndi Aroni,Ndi Samueli mwa iwo akuitanira dzina lace;Anaitana kwa Yehova, ndipo Iye anawayankha.

7. Iye analankhula nao mumtambo woti njo:Iwo anasunga mboni zace ndi malembawa anawapatsa,

8. Munawayankha, Yehova Mulungu wathu:Munawakhalira Mulungu wakuwakhululukira,Mungakhale munabwezera cilango pa zocita zao.

9. Mkwezeni Yehova Mulungu wathu,Ndipo gwadirani pa phiri lace loyera;Pakuti Yehova Mulungu wathu ndiye woyera.

Masalmo 99