Masalmo 98:8-9 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

8. Mitsinje iombe manja;Mapiri apfuule pamodzi mokondwera;

9. Pamaso pa Yehova, popeza akudza kudzaweruza dziko lapansi;Adzaweruza dziko lokhalamo anthu ndi cilungamo,Ndi mitundu ya anthu molunjika,

Masalmo 98