5. Ha! nchito zanu nzazikuru, Yehova,Zolingalira zanu nzozama ndithu.
6. Munthu wopulukira sacidziwa;Ndi munthu wopusa sacizindikira ici;
7. Cakuti pophuka oipa ngati msipu,Ndi popindula ocita zopanda pace;Citero kuti adzaonongeke kosatha:
8. Koma Inu, Yehova, muli m'mwamba ku nthawi yonse.
9. Pakuti, taonani, adani anu, Yehova,Pakuti, taonani, adani anu adzatayika;Ocita zopanda pace onse adzamwazika.