6. Kapena mliri woyenda mumdima,Kapena cionongeko cakuthera usana.
7. Pambali pako padzagwa cikwi,Ndi zikwi khumi pa dzanja lamanja lako;Sicidzakuyandikiza iwe.
8. Koma udzapenya ndi maso ako,Nudzaona kubwezera cilango oipa.
9. Popeza udati, Inu Yehova, ndinu pothawirapo pangaUdaika Wam'mwambamwamba cokhalamo cako;