Masalmo 82:1-3 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

1. Mulungu aima mu msonkhano wa Mulungu,Aweruza pakati pa milungu.

2. Mudzaweruza mosalunjika kufikira liti,Ndi kusamalira nkhope ya oipa?

3. Weruzani osauka ndi amasiye;Weruzani molungama ozunzika ndi osowa.

Masalmo 82