4. Udzikondweretsenso mwa Yehova;Ndipo iye adzakupatsa zokhumba mtima wako.
5. Pereka njira yako kwa Yehova; Khulupiriranso Iye, adzacicita.
6. Ndipo adzaonetsa cilungamo cako monga kuunika,Ndi kuweruza kwako monga usana.
7. Khala cete mwa Yehova, numlindirire Iye:Usabvutike mtima cifukwa ca iye wolemerera m'njira yace,Cifukwa ca munthu wakucita ciwembu.
8. Leka kupsa mtima, nutaye mkwiyo:Usabvutike mtima ungacite coipa,