Masalmo 22:1-3 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

1. Mulungu wanga, Mulungu wanga, mwandisiyiranji ine?Mukhaliranji kutali kwa cipulumutso canga, ndi kwa mau a kubuula kwanga?

2. Mulungu wanga, ndiitana usana, koma simubvomereza;Ndipo usiku, sindikhala cete.

3. Koma Inu ndinu woyera,Wakukhala m'malemekezo a Israyeli.

Masalmo 22