Masalmo 136:5-10 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

5. Amene analenga zakumwamba mwanzeru:Pakuti cifundo cace ncosatha.

6. Amene anayala dziko lapansi pamwamba pa madzi:Pakuti cifundo cace ncosatha.

7. Amene analenga miuni yaikuru:Pakuti cifundo cace ncosatha.

8. Dzuwa liweruze usana:Pakuti cifundo cace ncosatha.

9. Mwezi ndi nyenyezi ziweruze usiku;Pakuti cifundo cace ncosatha.

10. Iye amene anapandira Aaigupto ana ao oyamba:Pakuti cifundo cace ncosatha.

Masalmo 136