Masalmo 126:1-2 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

1. Pobweza Yehova ukapolo wa Ziyoni,Tinakhala ngati anthu akulota.

2. Pamenepo pakamwa pathu panadzala ndi kuseka,Ndi lilime lathu linapfuula mokondwera;Pamenepo anati mwa amitundu,Yehova anawacitira iwo zazikuru,

Masalmo 126