Marko 9:48-50 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

48. kumeneko mphutsi yao siikufa, ndi mota suzimidwa.

49. Pakuti onse adzathiridwa mcere wamoto,

50. Mcere uli wabwino; koma ngati mcere unasukuluka, mudzaukoleretsa ndi ciani? Khalani nao mcere mwa inu nokha, ndipo khalani ndi mtendere wina ndi mnzace.

Marko 9