48. kumeneko mphutsi yao siikufa, ndi mota suzimidwa.
49. Pakuti onse adzathiridwa mcere wamoto,
50. Mcere uli wabwino; koma ngati mcere unasukuluka, mudzaukoleretsa ndi ciani? Khalani nao mcere mwa inu nokha, ndipo khalani ndi mtendere wina ndi mnzace.