Marko 4:19 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

ndipo malabadiro a dziko lapansi, ndi cinyengo ca cuma, ndi kulakalaka kwa zinthu zina, zilowamo, zitsamwitsa mau, ndipo akhala opanda cipatso.

Marko 4

Marko 4:18-21