Marko 10:6-8 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

6. Koma kuyambira pa ciyambi ca malengedwe anawapanga mwamuna ndi mkazi.

7. Cifukwa cace mwamuna adzasiya atate wace ndi amai wace, ndipo adzaphatikizana ndi mkazi wace;

8. ndipo awiriwa adzakhala thupi limodzi: kotero kuti salinso awiri, koma thupi limodzi.

Marko 10