6. Koma kuyambira pa ciyambi ca malengedwe anawapanga mwamuna ndi mkazi.
7. Cifukwa cace mwamuna adzasiya atate wace ndi amai wace, ndipo adzaphatikizana ndi mkazi wace;
8. ndipo awiriwa adzakhala thupi limodzi: kotero kuti salinso awiri, koma thupi limodzi.