52. Ondida opanda cifukwa anandiinga ngati mbalame;
53. Anaononga moyo wanga m'dzenje, naponya mwala pamwambapaine;
54. Madzi anayenda pamwamba pa mutu panga, ndinati, dalikhidwa.
55. Ndinaitana dzina lanu, Yehova, ndiri m'dzenje lapansi;
56. Munamva mau anga; musabise khutu lanu popuma ndi popfuulaine.