Macitidwe 10:28 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

ndipo anati kwa iwo, Mudziwa inu nokha kuti sikuloledwa kwa munthu Myuda adziphatike kapena kudza kwa munthu wa mtundu wina; koma Mulungu anandionetsera ine ndisanenere ali yense ali munthu wamba kapena wonyansa;

Macitidwe 10

Macitidwe 10:19-32