Luka 9:13 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Koma anati kwa iwo, Muwapatse kudya ndinu. Koma anati, Ife tiribe mikate, koma isanu yokha, ndi nsomba ziwiri zokha; kapena timuke ife kukagulira anthu awa onse zakudya.

Luka 9

Luka 9:4-20