Luka 20:21 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo anamfunsa iye, nanena, Mphunzitisi, ife tidziwa kuti munena ndi kuphunzitsa kolunjika, ndi kusasamalira nkhope ya munthu, koma muphunzitsa njira ya Mulungu koonadi;

Luka 20

Luka 20:18-23